Notice: file_put_contents(): Write of 622 bytes failed with errno=28 No space left on device in /www/wwwroot/muzbon.net/system/url_helper.php on line 265
Lucius Banda - Nkokoma | Скачать MP3 бесплатно
Nkokoma

Nkokoma

Lucius Banda

Альбом: Crimes
Длительность: 4:54
Год: 2018
Скачать MP3

Текст песни

(Sley...)
(D-D-D-D-D-D-Dj Sley)
Heeeh, heeeh!

Munthu wobadwa mwa mkazi ali choncho
Lero aseke, mawa akukwiyire
Akulandile, pomwepo akuwingitse
Nsadalire, mtsamire kwa Jehovah
It is better, walk with you Jesus
It is safe, dwelling your pains
Insecure, leaving your house
Human beings have let me down

Pamene ndimkasauka, anali kukondwa nane
Akamanena za chuma chawo, ine nzichemelera
Koma lero ndamuziwa, mwini wa chuma chapansi
Sindizayenda ndi munthu
Nzayenda ndi Yesuyo

Nkokoma kuyenda ndi Ambuye
Nkwabwino kukhala ndi Yesu
Nkozuna kuyimbila Chauta
Nkwabwino kukhala m'nyumba yake
Nkokoma kuyenda ndi Ambuye
Nkwabwino kukhala ndi Yesu

Dziko lapansi lafika popweteka
Chilungamo chasanduka tchimo
Anthu akupha, achita kunyadila
Awo akuba, achita kubonisa
Tibisale nkhwapa mwanu Mbuye
I want to walk under your shadow
Ndifuna kuyimba, ndipate nzimu oyera
I want to live under your influence

Pamene ndimkasauka (aaa), anali kukondwa nane (aaa-aaa-aaa)
Akamanena za chuma chawo (aaa), ine nzichemelera
Koma lero ndamuziwa (aaa), mwini wa chuma chapansi (aaa-aaa-aaa)
Sindizayenda ndi munthu
Nzayenda ndi Yesuyo

Nkokoma kuyenda ndi Ambuye
Nkwabwino kukhala ndi Yesu
Nkozuna kuyimbila Chauta
Nkwabwino kukhala m'nyumba yake
Nkokoma kuyenda ndi Ambuye
Nkwabwino kukhala ndi Yesu

Chimpinduliranji kwa munthu wapadziko
Kupata zonse, kutaya moyo wake
Poti zapadziko sizikwanira
The more you have, the more you want to get
Solomon (heh-heh) adati ndizachabe (chabe)
Analinga (heh-heh) atakhala nazo (nazo)
Anali ndi zonse zofuna moyo wake
Koma ludzu wothetsa ndi Ambuye, yeah!

Nkokoma kuyenda ndi Ambuye (Aaah nkwabwino)
Nkwabwino kukhala ndi Yesu (Kuzuna, kuzuna, kuzuna mama)
Nkozuna kuyimbila Chauta (eeh, he-he-he-he-he-he-heh)
Nkwabwino kukhala m'nyumba yake (mkokomaaa!)
Nkokoma kuyenda ndi Ambuye (mkozuna, zuna)
Nkwabwino kukhala ndi Yesu

(Nkokoma, Nkokoma) nkokoma kuyenda ndi Yesu
Nko-nkoko-nkokoma, Oh!
Nkwabwino kukhala ndi Yesu
Nzofunika kukhala naye
Nkozuna kuyimbila Chauta (moyo wanga mama, weh)
Nkwabwino kukhala m'nyumba yake (ay, yeah-yeah-yeah ay, yoh-oh!)

Nkokoma kuyenda ndi Yesu (nkoko, kuyenda ndi Yesuyo)
Nkwabwino kukhala ndi Yesu (whoa Yesuyo)
Oh, oh-oh whoa
Nkokoma mamane weh (ooh)
Nkokoma ma-ma-ma-ma-ma-ma (weh oh-whoa)