Notice: file_put_contents(): Write of 618 bytes failed with errno=28 No space left on device in /www/wwwroot/muzbon.net/system/url_helper.php on line 265
Lucius Banda - Zisiike | Скачать MP3 бесплатно
Zisiike

Zisiike

Lucius Banda

Альбом: Yahwe
Длительность: 5:21
Год: 2012
Скачать MP3

Текст песни

Zakuti uyu wachoka ku Mpoto zisiyike
Zakuti uyunso wachoka ku M'mwela-nso zithe
Zakuti ndi Mlomwe, ndi Mchewa zichepe
Tonse ndi a Malawi likakhala dziko ndi lathu
Tonse ndi a Malawi, wolemera wosawuka
Tisateye nthawi kukhala wokhumbana mitundu

Musachedwe anzanga mkukumbana mitundu
Munthu aliyense ali ndi mphatso zake
Ndale zanu musamapangire pa guwa
Poti tchalitchi ndi la Mbuye Mulungu
Achisilamu amamutchula Allah
Akatolika amamutchula Yahweh
A dutch nawo amamutchula Jehovah
Koma Iye ndi m'modzi
Osabisala kuseli kwa mipingo

Zakuti nsilamu achoke pa udindo
Sizingatitchove abale musayiwale
Christu pamaso kumbali mkumapha
Kulibwino kukhala ndi nsilamu wachikondi
Mavuto anthu ndi uphawi si mipingo
Musabweze dziko m'manja mwa satana

Musachedwe anzanga mkukumbana mitundu
Munthu aliyense ali ndi mphatso zake
Ndale zanu musamapangire pa guwa
Poti tchalitchi ndi la Mbuye Mulungu
Awo achisilamu amamutchula Allah
Akatolika amamutchula Yahweh
A dutch nawo amamutchula Jehovah
Koma Iye ndi m'modzi
Oh usabisala kuseli kwa mipingo

Pakuti ku Mpoto kukanakhala ka dziko
Bwezi dzina lakelo likanakhala ndi poto
Abale Ifeyo ndi amodzi tikondane
Musalore anthu andale kukunamizani
Anthu akunja akalowa kumwamba
Ansembe, abusa muli busy kulimbana ndi ndale

Musachedwe anzanga mkukumbana mitundu
Munthu aliyense ali ndi mphatso zake
Ndale zanu musamapangire pa guwa
Poti tchalitchi ndi la Mbuye Mulungu
Achisilamu amamutchula Allah
Akatolika amamutchula Yahweh
A dutch nawo amamutchula Jehovah
Koma Iye ndi m'modzi
Oh osabisala kuseli kwa mipingo

Musachedwe anzanga mkukumbana mitundu
Munthu aliyense ali ndi mphatso zake
Ndale zanu musamapangire pa guwa
Poti tchalitchi ndi la Mbuye Mulungu
Achisilamu amamutchula Allah
Akatolika amamutchula Yahweh
A dutch nawo amamutchula Jehovah
Koma Iye ndi m'modzi
Osabisala kuseli kwa mipingo

Musachedwe anzanga mkukumbana mitundu
Munthu aliyense ali ndi mphatso zake
Ndale zanu musamapangire pa guwa
Poti tchalitchi ndi la Mbuye Mulungu
Awo achisilamu amamutchula Allah
Akatolika amamutchula Yahweh
A dutch nawo amamutchula Jehovah
Koma Iye ndi m'modzi
Osabisala kuseli kwa mipingo

(Achisilamu amamutchula Allah)
(Akatolika amamutchula Yahweh)
(A dutch nawo amamutchula Jehovah)